Mikango ikufunika njira zolera, yachuluka
Mathews Malata Bungwe la African Parks lonwe likuthandiza boma kusamalira nkhalango za Majete, Liwonde ndi Nkhotakota lati likulingalira zopempha boma kuti liyambe kugwiritsa ntchito ndondomeko “yakulera” pa mikango yomwe ati…