
Zisatikhuze MEC ikanila a Police nkhani ya Mithi
Bungwe la za chisankho mdziko la Malawi (Malawi Electoral Commission) lawuza bwalo la milandu ku Lilongwe kuti silinakadandaule kuli konse pa zomwe mkulu wodziwika pa masamba a mchezo a Facebook…
Bungwe la za chisankho mdziko la Malawi (Malawi Electoral Commission) lawuza bwalo la milandu ku Lilongwe kuti silinakadandaule kuli konse pa zomwe mkulu wodziwika pa masamba a mchezo a Facebook…
Anthu omwe akupikisana mmadela omwe muli zinduna kapena aphungu kale a chipani cholamula cha Malawi Congress (MCP) adandaula kuti masankho osankha oti azayimile pa zisankho za aphungu aku nyumba ya…
President Lazarus Chakwera wadabwitsa a Malawi pomwe anati iye akulimbana ndi katangale zomwe anthu ena sakukondwa nazo. Anthu ambiri pa tsamba la mchezo adabwa naye mtsogoleri wa dziko linoyi ngati…
Zadziwika kuti kampani yoyenga mafuta ya Addax Petroleum ndiyo inatumiza mkulu wa bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (MERA) a Henry Kachaje kupita ku Dubai kuti akachite zokambirana ndi mtsogoleri…
..anthu akugona ku Admarc Pamene boma kudzela ku unduna wa za ulimi likuziguguda pa ntima kuti likuthana ndi njala, ku Balaka anthu akugona ku nsika wa Admarc kudikila chimanga chomwe…
…feteleza mwalandira- Sam Kawale …Ombudsman akwiya ndi chipwirikiti Pamene nduna ya zaulimi a Sam Kawale amawuza atolankhani ku Lilongwe kuti ntchito yogawa zipangizo za ulimi yayenda bwino, anthu aku Ulongwe…
….A Chilima akuzadziwa ngati akudzayima pa 18 Juni, 2025 …Nyumba ya Malamulo ikudzayimitsidwa pa 16 Juni, 2025 …Kalembera wapadera achitika mu Novembala Nthawi yokonzekera chisankho cha mu 2025 yayambika pamene…
Anyamata otsatila zipani zomwe zili mgwirizano wa Tonse a Malawi Congress ndi UTM lachitatu sabata ino anakokana ma kholingo ndi kuswana ku malo aza malonda ku Chichiri mu mzinda wa…
Phindu lake ndi lotani? Kingsley Jassi walemba izi pa tsamba lake la mchezo Patatha zaka 8 boma likukambirana ndi company ya Globe Metals zotsekula mgodi wa Kanyika Niobium ku Mzimba,…
Mpingo wa Katoloka wati ndalama ndi zopeleka zonse zilandile la Mulungu sabata ino azipeleka kwa anthu omwe akhuzidwa ndi cyclone Freddy. Mkulu wa bungwe la ma Bishop a Katolika (Episcopal…