….A Chilima akuzadziwa ngati akudzayima pa 18 Juni, 2025 …Nyumba ya Malamulo ikudzayimitsidwa pa 16 Juni, 2025 …Kalembera wapadera achitika mu Novembala Nthawi yokonzekera chisankho cha mu...
Anyamata otsatila zipani zomwe zili mgwirizano wa Tonse a Malawi Congress ndi UTM lachitatu sabata ino anakokana ma kholingo ndi kuswana ku malo aza malonda ku Chichiri mu mzinda wa Blantyre....
Phindu lake ndi lotani? Kingsley Jassi walemba izi pa tsamba lake la mchezo Patatha zaka 8 boma likukambirana ndi company ya Globe Metals zotsekula mgodi wa Kanyika Niobium ku Mzimba, mbali ziwirizi...
Mpingo wa Katoloka wati ndalama ndi zopeleka zonse zilandile la Mulungu sabata ino azipeleka kwa anthu omwe akhuzidwa ndi cyclone Freddy. Mkulu wa bungwe la ma Bishop a Katolika (Episcopal...
Mathews Malata Bungwe la African Parks lonwe likuthandiza boma kusamalira nkhalango za Majete, Liwonde ndi Nkhotakota lati likulingalira zopempha boma kuti liyambe kugwiritsa ntchito ndondomeko...
Information and Technology Minister Gospel Kazako on Tuesday verbally attacked renowned Times TV presenter Brian Banda. In a shocking tirade as the reporter tried to probe who is in charge of...
Pamene a Malawi anali kulira chifukwa cha imfa za abale awo ku mliri wa Covid, anthu ogwira ntchito za boma anali pa chiphwando kugawana ndalama za Covid. Ombusdman Grace Malera anatulutsa...
The brutal killing of Tadala Chirwa, a 3 year old girl with albinism has attracted the attention of a global human rights lobby group- Amnesty International- which has asked Government to speer up...