Skip to content
November 9, 2025
  • Zim billionaire Wicknell, who is he?
  • APM to Break Record with 3 Million Votes
  • Kabambe accepts defeat
  • Panic and Intimidation as President Chakwera Targets Electoral Officers Over Election Loss
The Investigator News

The Investigator News

Random News
  • About Us
  • Business
  • Arts & Entertainment
  • Politics
  • iElections
  • Languages
    • Yao
    • Chichewa
    • Tumbuka
  • Sports
Headlines
  • Zim billionaire Wicknell, who is he?

    6 days ago6 days ago
  • Fuel Crisis: NOCMA’s missing K60billion for fuel

    12 months ago12 months ago
  • Joyce Banda says MEC, NRB has failed Malawians

    12 months ago12 months ago
  • ACB closes Sattar’s probe

    1 year ago1 year ago
  • Supreme Court frees Mutharika over K69 million legal bill

    1 year ago1 year ago
  • Resign, CDEDI, Opposition tells MEC Chair, CEO

    1 year ago1 year ago
  • Home
  • Languages

Languages

  • Chichewa
  • Mw Elections 2025
  • World

Mutharika apambana ndi 58%

admin2 months ago2 months ago02 mins

…Chakwera apeza 33.5% The Investigator Magazine itha kulengeza tsopano kuti mtsogoleri wakale wa dziko la Malawi a Peter Mutharika apambana chisankho cha udindo wa President ndi ma vote pafupi fupi…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

Ndemanga yathu: Ndondomeko ya Ana Ndi Zimbudzi ya Kongilesi nkutukwana a Malawi

admin4 months ago4 months ago03 mins

Pitani, kaberekani, MCP ilipira. Izi si Malembo Oyera ayi, koma ndilo lonjezo latsopano kwambiri m’ndondomeko ya MCP ya kampeni yakuti a Malawi awavotele pa 16 Sepetember pano. A President Lazarus Chakwera…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

Boma likuganizila kuphazi-Alimi a fodya

admin5 months ago5 months ago04 mins

..fodya chaka chino wochepa kale ndi 60 million kgs …25% yotenga boma idzutsa mapiri pa chigwa ..nzeru zopezela ndalama zatha ku boma Munthu yekha yemwe amaganizila kuphazi osati ubongo ndiye…

Read More
  • Chichewa
  • World

Zisatikhuze MEC ikanila a Police nkhani ya Mithi

admin7 months ago7 months ago02 mins

Bungwe la za chisankho mdziko la Malawi (Malawi Electoral Commission) lawuza bwalo la milandu ku Lilongwe kuti silinakadandaule kuli konse pa zomwe mkulu wodziwika pa masamba a mchezo a Facebook…

Read More
  • Chichewa
  • Politics
  • World

MCP isintha zisankho kuti zikomele nduna- Opikisana

admin7 months ago7 months ago02 mins

Anthu omwe akupikisana mmadela omwe muli zinduna kapena aphungu kale a chipani cholamula cha Malawi Congress (MCP) adandaula kuti masankho osankha oti azayimile pa zisankho za aphungu aku nyumba ya…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

Chakwera adabwitsa anthu pa za katangale

admin8 months ago8 months ago03 mins

President Lazarus Chakwera wadabwitsa a Malawi pomwe anati iye akulimbana ndi katangale zomwe anthu ena sakukondwa nazo. Anthu ambiri pa tsamba la mchezo adabwa naye mtsogoleri wa dziko linoyi ngati…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

 NOCMA, MERA akolezera chipwirikiti cha mafuta: Kampani ya Addax itchulidwa  

admin10 months ago10 months ago09 mins

Zadziwika kuti kampani yoyenga mafuta ya Addax Petroleum ndiyo inatumiza mkulu wa bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (MERA) a Henry Kachaje kupita ku Dubai kuti akachite zokambirana ndi mtsogoleri…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

Ku Balaka njala yavuta

admin2 years ago2 years ago02 mins

..anthu akugona ku Admarc Pamene boma kudzela ku unduna wa za ulimi likuziguguda pa ntima kuti likuthana ndi njala, ku Balaka anthu akugona ku nsika wa Admarc kudikila chimanga chomwe…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

Feteleza kulibe, atelo anthu

admin2 years ago2 years ago04 mins

…feteleza mwalandira- Sam Kawale …Ombudsman akwiya ndi chipwirikiti Pamene nduna ya zaulimi a Sam Kawale amawuza atolankhani ku Lilongwe kuti ntchito yogawa zipangizo za ulimi yayenda bwino, anthu aku Ulongwe…

Read More
  • Chichewa
  • Languages
  • World

MEC iyamba kukonzekera zisankho  za 2025

admin2 years ago2 years ago09 mins

….A Chilima akuzadziwa ngati akudzayima pa 18 Juni, 2025 …Nyumba ya Malamulo ikudzayimitsidwa pa 16 Juni, 2025 …Kalembera wapadera achitika mu Novembala Nthawi yokonzekera chisankho cha mu 2025 yayambika pamene…

Read More
  • 1
  • 2

Recent Posts

  • Zim billionaire Wicknell, who is he?
  • APM to Break Record with 3 Million Votes
  • Kabambe accepts defeat
  • Panic and Intimidation as President Chakwera Targets Electoral Officers Over Election Loss
  • Mutharika apambana ndi 58%

Subscribe to our Online Magazine

Recent Posts

  • Zim billionaire Wicknell, who is he?
  • APM to Break Record with 3 Million Votes
  • Kabambe accepts defeat
  • Panic and Intimidation as President Chakwera Targets Electoral Officers Over Election Loss
  • Mutharika apambana ndi 58%

The Investigator

creating a free, just and accountable society

Address

KBM Associates Ltd, Blackdown Close, London, N2 8JF – United Kingdom

Malawi:

Centre for Public Accountability- Open Malawi, Old Town Mall, Lilongwe.

The Investigator

editor@ theinvestigator.news director@openmalawi. org Mobile: Main – Whatsapp only +265 9999 57331 Malawi Office Lughano: 265 996 990 011 UK and Worldwide: WhatsApp only +44 7949631446.

Web: www.theinvestigator.news or www.openmalawi.org