Pamene a Malawi anali kulira chifukwa cha imfa za abale awo ku mliri wa Covid, anthu ogwira ntchito za boma anali pa chiphwando kugawana ndalama za Covid. Ombusdman Grace Malera anatulutsa lipoti lomwe likuwonetsa komwe ndalama za Covid zinalowela pomwe ena anali kuthatha ndi moyo.
Welengani nkhaniyi mu Chichewa, mu Chitumbuka ndinso mu chi Yao mmagazine ya The Investigator yomwe yatuluka lero……
Anyamata otsatila zipani zomwe zili mgwirizano wa Tonse a Malawi Congress ndi UTM lachitatu sabata ino anakokana ma kholingo ndi kuswana ku malo aza malonda ku Chichiri mu mzinda wa Blantyre....
Phindu lake ndi lotani? Kingsley Jassi walemba izi pa tsamba lake la mchezo Patatha zaka 8 boma likukambirana ndi company ya Globe Metals zotsekula mgodi wa Kanyika Niobium ku Mzimba, mbali ziwirizi...
Mpingo wa Katoloka wati ndalama ndi zopeleka zonse zilandile la Mulungu sabata ino azipeleka kwa anthu omwe akhuzidwa ndi cyclone Freddy. Mkulu wa bungwe la ma Bishop a Katolika (Episcopal...