
Mutharika apambana ndi 58%
…Chakwera apeza 33.5% The Investigator Magazine itha kulengeza tsopano kuti mtsogoleri wakale wa dziko la Malawi a Peter Mutharika apambana chisankho cha udindo wa President ndi ma vote pafupi fupi…
…Chakwera apeza 33.5% The Investigator Magazine itha kulengeza tsopano kuti mtsogoleri wakale wa dziko la Malawi a Peter Mutharika apambana chisankho cha udindo wa President ndi ma vote pafupi fupi…
Pitani, kaberekani, MCP ilipira. Izi si Malembo Oyera ayi, koma ndilo lonjezo latsopano kwambiri m’ndondomeko ya MCP ya kampeni yakuti a Malawi awavotele pa 16 Sepetember pano. A President Lazarus Chakwera…
..fodya chaka chino wochepa kale ndi 60 million kgs …25% yotenga boma idzutsa mapiri pa chigwa ..nzeru zopezela ndalama zatha ku boma Munthu yekha yemwe amaganizila kuphazi osati ubongo ndiye…
Bungwe la za chisankho mdziko la Malawi (Malawi Electoral Commission) lawuza bwalo la milandu ku Lilongwe kuti silinakadandaule kuli konse pa zomwe mkulu wodziwika pa masamba a mchezo a Facebook…
Anthu omwe akupikisana mmadela omwe muli zinduna kapena aphungu kale a chipani cholamula cha Malawi Congress (MCP) adandaula kuti masankho osankha oti azayimile pa zisankho za aphungu aku nyumba ya…
President Lazarus Chakwera wadabwitsa a Malawi pomwe anati iye akulimbana ndi katangale zomwe anthu ena sakukondwa nazo. Anthu ambiri pa tsamba la mchezo adabwa naye mtsogoleri wa dziko linoyi ngati…
Zadziwika kuti kampani yoyenga mafuta ya Addax Petroleum ndiyo inatumiza mkulu wa bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (MERA) a Henry Kachaje kupita ku Dubai kuti akachite zokambirana ndi mtsogoleri…
..anthu akugona ku Admarc Pamene boma kudzela ku unduna wa za ulimi likuziguguda pa ntima kuti likuthana ndi njala, ku Balaka anthu akugona ku nsika wa Admarc kudikila chimanga chomwe…
…feteleza mwalandira- Sam Kawale …Ombudsman akwiya ndi chipwirikiti Pamene nduna ya zaulimi a Sam Kawale amawuza atolankhani ku Lilongwe kuti ntchito yogawa zipangizo za ulimi yayenda bwino, anthu aku Ulongwe…
….A Chilima akuzadziwa ngati akudzayima pa 18 Juni, 2025 …Nyumba ya Malamulo ikudzayimitsidwa pa 16 Juni, 2025 …Kalembera wapadera achitika mu Novembala Nthawi yokonzekera chisankho cha mu 2025 yayambika pamene…